Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 27:15 - Buku Lopatulika

15 ndipo pogwidwa nayo ngalawa, yosakhoza kupitanso mokomana nayo mphepo, tidangoleka, ndipo tinangotengedwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 ndipo pogwidwa nayo ngalawa, yosakhoza kupitanso mokomana nayo mphepo, tidangoleka, ndipo tinangotengedwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Idaomba chombo chija, ndiye popeza kuti sitidathe kuchiwongolera moyang'anana ndi mphepoyo, tidaigonjera nkungotengedwa nayo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Mphepo yamkunthoyo inawomba sitima ija ndipo sinathe kulimbana nayo, kotero ife tinayigonjera ndi kuyamba kutengedwa nayo.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 27:15
4 Mawu Ofanana  

Koma patapita pang'ono idaombetsa kuchokerako mphepo ya namondwe, yonenedwa Yurakulo;


Ndipo popita kuseri kwa chisumbu chaching'ono dzina lake Kauda, tinakhoza kumangitsa bwato koma movutika;


Koma pofika usiku wakhumi ndi chinai, potengedwa ife kwina ndi kwina m'nyanja ya Adriya, pakati pa usiku amalinyero anazindikira kuti analikuyandikira kumtunda;


Taonani, zombonso, zingakhale zazikulu zotere, nkutengedwa ndi mphepo zolimba, zipotozeka ndi tsigiro laling'ono ndithu kumene kulikonse afuna wogwira tsigiro.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa