Machitidwe a Atumwi 26:31 - Buku Lopatulika31 ndipo atapita padera analankhula wina ndi mnzake, nanena, Munthu uyu sanachite kanthu koyenera imfa, kapena nsinga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 ndipo atapita padera analankhula wina ndi mnzake, nanena, Munthu uyu sanachita kanthu koyenera imfa, kapena nsinga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Atachokapo adauzana kuti, “Munthuyu sakuchita chilichonse choyenera kumuphera kapena kumponyera m'ndende.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Inatuluka mʼchipindamo, ndipo pamene imayankhula inati, “Munthu uyu sanachite kanthu koyenera kuphedwa kapena kumangidwa.” Onani mutuwo |