Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 26:27 - Buku Lopatulika

27 Mfumu Agripa, mukhulupirira aneneri kodi? Ndidziwa kuti muwakhulupirira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Mfumu Agripa, mukhulupirira aneneri kodi? Ndidziwa kuti muwakhulupirira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Inu mfumu Agripa, kodi mumakhulupirira mau a aneneri? Ndikudziŵa kuti mumaŵakhulupirira.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Mfumu Agripa, kodi mumakhulupirira mawu a aneneri? Ine ndikudziwa kuti mumakhulupirira.”

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 26:27
3 Mawu Ofanana  

Pakuti mfumuyo idziwa izi, kwa iye imene ndilankhula nayonso mosaopa: pakuti ndidziwadi kuti kulibe kanthu ka izi kadambisikira; pakuti ichi sichinachitike m'tseri.


Ndipo Agripa anati kwa Paulo, Ndi kundikopa pang'ono ufuna kundiyesera Mkhristu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa