Machitidwe a Atumwi 26:24 - Buku Lopatulika24 Koma pakudzikanira momwemo, Fesito anati ndi mau aakulu, Uli wamisala Paulo; kuwerengetsa kwako kwakuchititsa misala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Koma pakudzikanira momwemo, Fesito anati ndi mau akulu, Uli wamisala Paulo; kuwerengetsa kwako kwakuchititsa misala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Pamene Paulo ankadziteteza ku zomnenezazo, Fesito adanena mokweza mau kuti, “Misalatu imeneyi, iwe Paulo! Kuphunziritsa kwako kukukupengetsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Paulo akudziteteza, Festo anakweza mawu nati, “Wazungulira mutu Paulo! Kuphunzira kwako kwakuchititsa misala.” Onani mutuwo |