Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 26:21 - Buku Lopatulika

21 Chifukwa cha izi Ayuda anandigwira mu Kachisi, nayesa kundipha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Chifukwa cha izi Ayuda anandigwira m'Kachisi, nayesa kundipha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Chifukwa cha zimenezi Ayuda adandigwira m'Nyumba ya Mulungu nafuna kundipha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Ichi nʼchifukwa chake Ayuda anandigwira mʼbwalo la Nyumba ya Mulungu nafuna kundipha.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 26:21
5 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene masiku asanu ndi awiri anati amalizidwe, Ayuda a ku Asiya pomuona iye mu Kachisi, anautsa khamu lonse la anthu, namgwira,


Ndipo adamumva kufikira mau awa; ndipo anakweza mau ao nanena, Achoke padziko lapansi munthu wotere; pakuti sayenera iye kukhala ndi moyo.


nampempha kuti mlandu wake wa Paulo uipe, kuti amuitane iye adze ku Yerusalemu; iwo amchitira chifwamba kuti amuphe panjira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa