Machitidwe a Atumwi 26:19 - Buku Lopatulika19 Potero, Mfumu Agripa, sindinakhale ine wosamvera masomphenya a Kumwamba; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Potero, Mfumu Agripa, sindinakhala ine wosamvera masomphenya a Kumwamba; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 “Nchifukwa chake, mfumu Agripa, sindidakane kumvera zimene Mulungu adandiwonetsa m'masomphenyazo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 “Nʼchifukwa chake Mfumu Agripa, sindinakane kumvera masomphenya wochokera kumwamba. Onani mutuwo |