Machitidwe a Atumwi 26:17 - Buku Lopatulika17 ndi kukulanditsa kwa anthu, ndi kwa amitundu, amene Ine ndikutuma kwa iwo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 ndi kukulanditsa kwa anthu, ndi kwa amitundu, amene Ine ndikutuma kwa iwo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ndidzakulanditsa kwa anthu a mtundu wako, ndiponso kwa anthu a mitundu ina kumene ndikukutuma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ine ndidzakulanditsa mʼmanja mwa anthu a mtundu wako ndiponso mwa anthu a mitundu ina. Ine ndikukutuma kwa iwo, Onani mutuwo |