Machitidwe a Atumwi 26:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo pamene tidagwa pansi tonse, ndinamva mau akunena kwa ine m'chinenedwe cha Chihebri, Saulo, Saulo, undilondalonderanji Ine? Nkukuvuta kutsalima pachotwikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo pamene tidagwa pansi tonse, ndinamva mau akunena kwa ine m'chinenedwe cha Chihebri, Saulo, Saulo, undilondalonderanji Ine? Nkukuvuta kutsalima pachotwikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tonse tidagwa pansi, ndipo ine ndidamva mau ondiwuza pa Chiyuda kuti, ‘Saulo, Saulo, ukundizunziranji? Ukungodzipweteka wekha ngati ng'ombe yoponda zidyali pa chobayira.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Tonse tinagwa pansi ndipo ndinamva mawu mʼChihebri akuti, ‘Saulo, Saulo chifukwa chiyani ukundizunza Ine? Nʼkovuta kulimbikira mtunda wopanda madzi.’ ” Onani mutuwo |