Machitidwe a Atumwi 25:3 - Buku Lopatulika3 nampempha kuti mlandu wake wa Paulo uipe, kuti amuitane iye adze ku Yerusalemu; iwo amchitira chifwamba kuti amuphe panjira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 nampempha kuti mlandu wake wa Paulo uipe, kuti amuitane iye adze ku Yerusalemu; iwo amchitira chifwamba kuti amuphe panjira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 kuti aŵakomere mtima pakumtumiza Paulo ku Yerusalemu. Adaatero chifukwa anali atapangana zomulalira Paulo kuti amuphe pa njira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iwo anamupempha Festo kuti awakomere mtima potumiza Paulo ku Yerusalemu, pakuti anali atakonzekera chiwembu kuti amuphe Pauloyo pa njira. Onani mutuwo |