Machitidwe a Atumwi 24:4 - Buku Lopatulika4 Koma kuti ndingaonjeze kukulemetsani ndikupemphani mutimvere mwachidule ndi chifatso chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Koma kuti ndingaonjeze kukulemetsani ndikupemphani mutimvere mwachidule ndi chifatso chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pepani sindikufuna kukutayitsani nthaŵi, komabe ndimapempha kuti mundikomere mtima, mungomvapo mau athuŵa mwachidule. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Koma kuti tisakuchedwetseni, ndikupempha kuti mwa kuleza mtima kwanu mutimvere ife. Onani mutuwo |