Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 24:20 - Buku Lopatulika

20 Kapena iwo amene ali kunowa anene anapeza chosalungama chotani, poimirira ine pamaso pabwalo la akulu a milandu,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Kapena iwo amene ali kunowa anene anapeza chosalungama chotani, poimirira ine pamaso pa bwalo la akulu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Kapena omwe ali panoŵa anene ngati adandipeza cholakwa pamene ndinali m'Bwalo lao Lalikulu lamilandu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Kapena awa amene ali panowa anene mlandu umene anapeza mwa ine, pamene ndinayima pamaso pa Bwalo lawo Lalikulu.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 24:20
4 Mawu Ofanana  

Nati iye, Sindimavute Israele ine ai, koma inu ndi nyumba ya atate wanu; popeza munasiya malamulo a Yehova, ndi kutsata Abaala.


Pamenepo anthu awa anati, Sitidzamtola chifukwa chilichonse Daniele amene, tikapanda kumtola ichi pa chilamulo cha Mulungu wake.


koma Ine ndinena kwa inu, kuti yense wokwiyira mbale wake wopanda chifukwa adzakhala wopalamula mlandu; ndipo amene adzanena ndi mbale wake, Wopanda pake iwe, adzakhala wopalamula mlandu wa akulu: koma amene adzati, Chitsiru iwe: adzakhala wopalamula Gehena wamoto.


Ndipo iye ananena nao, Yehova ali mboni yanu, ndi wodzozedwa wake ali mboni lero kuti simunapeze kanthu m'dzanja langa. Nati iwo, Iye ali mboni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa