Machitidwe a Atumwi 24:19 - Buku Lopatulika19 koma panali Ayuda ena a ku Asiya, ndiwo mwenzi atakhala pano pamaso panu ndi kundinenera, ngati ali nako kanthu kotsutsa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 koma panali Ayuda ena a ku Asiya, ndiwo mwenzi atakhala pano pamaso panu ndi kundinenera, ngati ali nako kanthu kotsutsa ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Koma kunali Ayuda ena a ku Asiya. Iwowo akadayenera kukhala pano pamaso panu kudzandineneza okha ngati ali nane nkanthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Koma pali Ayuda ena ochokera ku Asiya, amene amayenera kukhala pano pamaso panu, kundiyimba mlandu ngati ali ndi kalikonse konditsutsa ine. Onani mutuwo |