Machitidwe a Atumwi 24:18 - Buku Lopatulika18 popereka izi anandipeza woyeretsedwa mu Kachisi, wopanda khamu la anthu, kapena phokoso; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 popereka izi anandipeza woyeretsedwa m'Kachisi, wopanda khamu la anthu, kapena phokoso; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Pamene ndinkachita zimenezi, iwo adandipeza m'Nyumba ya Mulungu nditachita mwambo wakudziyeretsa. Panalibe konse khamu la anthu kapena chipolowe ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pamene ndinkachita zimenezi, iwo anandipeza mʼbwalo la Nyumba ya Mulungu nditachita mwambo wodziyeretsa. Panalibe gulu la anthu kapena kuti ndimachita za chisokonezo chilichonse. Onani mutuwo |