Machitidwe a Atumwi 24:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo zitapita zaka zambiri ndinadza kutengera mtundu wanga zachifundo, ndi zopereka; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo zitapita zaka zambiri ndinadza kutengera mtundu wanga zachifundo, ndi zopereka; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 “Tsono nditakhala kwina zaka zingapo, ndidabwera kudzatula zopereka zachifundo kwa anthu a mtundu wanga, ndiponso kudzapereka nsembe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 “Patapita zaka zambiri, ndinabwera ku Yerusalemu kudzapereka mphatso kwa anthu osauka a mtundu wanga komanso kudzapereka nsembe. Onani mutuwo |