Machitidwe a Atumwi 24:16 - Buku Lopatulika16 M'menemonso ndidziyesera ndekha ndikhale nacho nthawi zonse chikumbumtima chosanditsutsa cha kwa Mulungu ndi kwa anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 M'menemonso ndidziyesera ndekha ndikhale nacho nthawi zonse chikumbu mtima chosanditsutsa cha kwa Mulungu ndi kwa anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Nchifukwa chake inenso ndimayesetsa nthaŵi zonse kukhala ndi mtima wangwiro pamaso pa Mulungu, ndi pamaso pa anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Kotero ine ndimayesetsa kuti ndikhale ndi chikumbumtima chosanditsutsa pamaso pa Mulungu ndi anthu onse. Onani mutuwo |