Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 24:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo sangathe kukutsimikizirani zimene andinenera ine tsopano.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo sangathe kukutsimikizirani zimene andinenera ine tsopano.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Iwoŵa sangakutsimikizireni zimene akundinenezazi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Ndipo sangathe kupereka umboni wa mlandu umene akundiyimba inewu.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 24:13
4 Mawu Ofanana  

Pokhala iye mu Chipata cha Benjamini, kapitao wa alonda anali kumeneko, dzina lake Iriya, mwana wa Selemiya, mwana wa Hananiya; ndipo iye anamgwira Yeremiya mneneri, nati, Ulinkupandukira kwa Ababiloni.


Pamenepo anthu awa anati, Sitidzamtola chifukwa chilichonse Daniele amene, tikapanda kumtola ichi pa chilamulo cha Mulungu wake.


Ndipo m'mene anafika iye, Ayuda adatsikawo ku Yerusalemu anaimirira pomzinga iye, namnenera zifukwa zambiri ndi zazikulu, zimene sanathe kuzitsimikiza;


ndi kukhala nacho chikumbumtima chabwino, kuti umo akunenerani, iwo akunenera konama mayendedwe anu abwino mu Khristu akachitidwe manyazi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa