Machitidwe a Atumwi 23:8 - Buku Lopatulika8 Pakutitu Asaduki anena kuti kulibe kuuka kwa akufa, kapena mngelo, kapena mzimu; koma Afarisi avomereza ponse pawiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pakutitu Asaduki anena kuti kulibe kuuka kwa akufa, kapena mngelo, kapena mzimu; koma Afarisi avomereza ponse pawiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Paja Asaduki amati anthu sadzauka kwa akufa, ndiponso kuti kulibe angelo kapena mizimu. Koma Afarisi amakhulupirira zonsezi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Asaduki amati kulibe kuuka kwa akufa, kulibenso ngakhale angelo kapena mizimu, koma Afarisi amakhulupirira zonsezi. Onani mutuwo |