Machitidwe a Atumwi 23:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo pamene adatero, kunakhala chilekano pakati pa Afarisi ndi Asaduki; ndipo osonkhanawo anagawikana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo pamene adatero, kunakhala chilekano pakati pa Afarisi ndi Asaduki; ndipo osonkhanawo anagawikana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Atanena zimenezi, Afarisi ndi Asaduki aja adayamba kukangana, ndipo msonkhano udagaŵana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iye atanena zimenezi, mkangano unabuka pakati pa Afarisi ndi Asaduki mpaka anthu kugawikana. Onani mutuwo |