Machitidwe a Atumwi 23:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo iwo akuimirirako anati, Ulalatira kodi mkulu wa ansembe wa Mulungu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo iwo akuimirirako anati, Ulalatira kodi mkulu wa ansembe wa Mulungu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Apo amene adaaimirira pafupi adauza Paulo kuti, “Bwanji ukunena zachipongwe kwa mkulu wa ansembe wa Mulungu?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Anthu amene anayimirira pafupi ndi Paulo anati, “Bwanji ukunyoza mkulu wa ansembe wa Mulungu?” Onani mutuwo |