Machitidwe a Atumwi 23:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo anati, Ayuda anapangana kuti akufunseni mutsike naye Paulo mawa kubwalo la akulu a milandu, monga ngati mufuna kufunsitsa za iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo anati, Ayuda anapangana kuti akufunseni mutsike naye Paulo mawa kubwalo la milandu, monga ngati mufuna kufunsitsa za iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Iyeyo adati, “Ayuda ena apangana zodzakupemphani kuti mupite ndi Paulo ku Bwalo lao Lalikulu lamilandu maŵa, ngati kuti iwowo akufuna kufunsitsa bwino za mlandu wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Mnyamatayo anati, “Ayuda agwirizana zoti akupempheni kuti mawa mubwere ndi Paulo ku Bwalo Lalikulu, ngati kuti akufuna kudziwa bwino za iye. Onani mutuwo |