Machitidwe a Atumwi 23:18 - Buku Lopatulika18 Pamenepo ndipo anamtenga, napita naye kwa kapitao wamkulu, nati, Wam'nsingayo Paulo anandiitana, nandipempha ndidze naye mnyamata uyu kwa inu, ali nako kanthu kakulankhula ndi inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pamenepo ndipo anamtenga, napita naye kwa kapitao wamkulu, nati, Wam'nsingayo Paulo anandiitana, nandipempha ndidze naye mnyamata uyu kwa inu, ali nako kanthu kakulankhula ndi inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Iye adamtengadi mnyamatayo kupita naye kwa mkulu wa asilikali, namuuza kuti, “Mkaidi uja Paulo anandiitana, nandipempha kuti ndibwere ndi mnyamatayu kwa inu, akuti ali nanu ndi mau.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Anamutengadi mnyamatayo napita naye kwa mkulu wa asilikali uja, nati, “Wamʼndende uja Paulo anandiyitana, nandipempha kuti ndibweretse mnyamatayu kwa inu chifukwa ali ndi kanthu koti akuwuzeni.” Onani mutuwo |