Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 22:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo pakufuula iwo, ndi kutaya zovala zao, ndi kuwaza fumbi mumlengalenga,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo pakufuula iwo, ndi kutaya zovala zao, ndi kuwaza fumbi mumlengalenga,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Iwowo ankafuula nkumazunguza malaya ao, namawaza fumbi kumwamba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Akufuwula ndi kuponya zovala zawo ndi kuwaza fumbi kumwamba,

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 22:23
6 Mawu Ofanana  

Chomwecho Davide ndi anthu ake anapita m'njira, ndipo Simei analambalala paphiri popenyana naye, namuka natukwana, namponya miyala, nawaza fumbi.


Inde, poyendanso chitsiru panjira, nzeru yake imthera ndipo angoti kwa onse kuti, Ndine chitsiru.


Ndipo pamene Yesu analikuyenda m'mbali mwa nyanja ya Galileya, anaona abale awiri, Simoni wonenedwa Petro, ndi Andrea, mbale wake, analikuponya khoka m'nyanja; popeza anali asodzi a nsomba.


Ndipo ndinawalanga kawirikawiri m'masunagoge onse, ndi kuwakakamiza anene zamwano; ndipo pakupsa mtima kwakukulu pa iwo ndinawalondalonda ndi kuwatsata ngakhale kufikira kumizinda yakunja.


inu amene munalandira chilamulo monga chidaikidwa ndi angelo, ndipo simunachisunge.


ndipo anamtaya kunja kwa mzinda, namponya miyala; ndipo mbonizo zinaika zovala zao pa mapazi a mnyamata dzina lake Saulo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa