Machitidwe a Atumwi 22:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo pakufuula iwo, ndi kutaya zovala zao, ndi kuwaza fumbi mumlengalenga, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo pakufuula iwo, ndi kutaya zovala zao, ndi kuwaza fumbi mumlengalenga, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Iwowo ankafuula nkumazunguza malaya ao, namawaza fumbi kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Akufuwula ndi kuponya zovala zawo ndi kuwaza fumbi kumwamba, Onani mutuwo |