Machitidwe a Atumwi 22:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo anati kwa ine, Pita; chifukwa Ine ndidzakutuma iwe kunka kutali kwa amitundu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo anati kwa ine, Pita; chifukwa Ine ndidzakutuma iwe kunka kutali kwa amitundu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Apo Ambuye adandiwuza kuti, ‘Nyamuka, chifukwa Ine ndidzakutuma kutali kwa anthu a mitundu ina.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Pamenepo Ambuye anandiwuza kuti, “Nyamuka; Ine ndidzakutuma kutali kwa anthu a mitundu ina.” Onani mutuwo |