Machitidwe a Atumwi 22:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo tsopano uchedweranji? Tauka, nubatizidwe ndi kusamba kuchotsa machimo ako, nuitane pa dzina lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo tsopano uchedweranji? Tauka, nubatizidwe ndi kusamba kuchotsa machimo ako, nuitane pa dzina lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Nanga tsono ukuchedweranji? Dzuka ndi kutama dzina lake mopemba, ubatizidwe ndi kusambitsidwa kuti machimo ako achoke.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndipo tsopano ukudikira chiyani? Dzuka ndi kutama dzina la Ambuye mopemba, ubatizidwe ndi kuchotsa machimo ako.’ Onani mutuwo |