Machitidwe a Atumwi 22:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo anati, Mulungu wa makolo athu anakusankhiratu udziwe chifuniro chake, nuone Wolungamayo, numve mau otuluka m'kamwa mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo anati, Mulungu wa makolo athu anakusankhiratu udziwe chifuniro chake, nuone Wolungamayo, numve mau otuluka m'kamwa mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tsono adandiwuza kuti, ‘Mulungu wa makolo athu adakusankha kuti udziŵe zimene Iye akufuna, uwone Wolungama uja, ndipo umve mau ake olankhula nawe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Ndipo iye anati, ‘Mulungu wa makolo athu wakusankha iwe kuti udziwe chifuniro chake ndi kuona Wolungamayo ndi kumva mawu ochokera pakamwa pake. Onani mutuwo |