Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 22:13 - Buku Lopatulika

13 anadza kwa ine, ndipo poimirirapo anati kwa ine, Saulo, mbale, penyanso. Ndipo ine, ora lomweli ndinampenya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 anadza kwa ine, ndipo poimirirapo anati kwa ine, Saulo, mbale, penyanso. Ndipo ine, ora lomweli ndinampenya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Iyeyo adafika nadzaimirira pafupi nane, nkundiwuza kuti, ‘Mbale wanga Saulo, yambanso kupenya.’ Nthaŵi yomweyo ndidayambadi kupenya ndipo iyeyo ndidamuwona.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Iye anayimirira pafupi nane nati, ‘Mʼbale Saulo, penyanso!’ Ndipo nthawi yomweyo ndinapenya ndikumuona iyeyo.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 22:13
2 Mawu Ofanana  

osatinso monga kapolo, koma woposa kapolo, mbale wokondedwa, makamaka ndi ine, koma koposa nanga ndi iwe, m'thupi, ndiponso mwa Ambuye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa