Machitidwe a Atumwi 22:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo popeza sindinapenye, chifukwa cha ulemerero wa kuunikako, anandigwira dzanja iwo amene anali ndi ine, ndipo ndinafika ku Damasiko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo popeza sindinapenya, chifukwa cha ulemerero wa kuunikako, anandigwira dzanja iwo amene anali ndi ine, ndipo ndinafika ku Damasiko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Sindidathe kupenyanso chifukwa cha kuŵala kwakukulu kuja, nchifukwa chake anzanga aja adachita kundigwira pa dzanja nkumanditsogolera mpaka kukaloŵa m'Damasiko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Anzanga anandigwira dzanja kupita nane ku Damasiko, popeza kuwala kunja kunandichititsa khungu. Onani mutuwo |