Machitidwe a Atumwi 21:23 - Buku Lopatulika23 Chifukwa chake uchite ichi tikuuza iwe; tili nao amuna anai amene anawinda; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Chifukwa chake uchite ichi tikuuza iwe; tili nao amuna anai amene anawinda; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Ndiye inu, muchite zimene tikuuzeni ife. Tili ndi amuna anai pano amene adachita lumbiro kwa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 tsono iwe chita zimene ife tikuwuze. Tili nawo amuna anayi pano amene anachita lumbiro kwa Mulungu. Onani mutuwo |