Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 21:22 - Buku Lopatulika

22 Nchiyani tsono? Adzamva ndithu kuti wafika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Nchiyani tsono? Adzamva ndithu kuti wafika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Tsono pamenepa titani? Kumva adzamva ndithu kuti mwafika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Nanga pamenepa ife titani? Iwo adzamva ndithu kuti iwe wabwera,

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 21:22
6 Mawu Ofanana  

Ndipo khamu lonse linatonthola; ndipo anamvera Barnabasi ndi Paulo alikubwerezanso zizindikiro ndi zozizwitsa zimene Mulungu anachita nao pa amitundu.


Pamenepo chinakomera atumwi ndi akulu ndi Mpingo wonse kusankha anthu a m'gulu lao, ndi kuwatumiza ku Antiokeya ndi Paulo ndi Barnabasi; ndiwo Yudasi wotchedwa Barsabasi, ndi Silasi, akulu a mwa abale; ndipo analembera mau natumiza ndi iwo:


Ndipo ena anafuula kanthu kena, ena kanthu kena; pakuti msonkhanowo unasokonezeka; ndipo unyinji sunadziwe chifukwa chake cha kusonkhana.


ndipo anamva za iwe, kuti uphunzitsa Ayuda onse a kwa amitundu apatukane naye Mose, ndi kuti asadule ana ao, kapena asayende monga mwa miyambo.


Chifukwa chake uchite ichi tikuuza iwe; tili nao amuna anai amene anawinda;


Kuli chiyani tsono? Ndidzapemphera ndi mzimu, koma ndidzapempheranso ndi chidziwitso changa; ndidzaimba ndi mzimu, koma ndidzaimbanso ndi chidziwitso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa