Machitidwe a Atumwi 21:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo m'mawa mwake Paulo analowa nafe kwa Yakobo; ndi akulu onse anali pomwepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo m'mawa mwake Paulo analowa nafe kwa Yakobo; ndi akulu onse anali pomwepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 M'maŵa mwake Paulo adatitenga kupita kwa Yakobe. Akuluampingo onse anali kumeneko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Mmawa mwake Paulo pamodzi ndi ife tonse tinapita kwa Yakobo, ndipo akulu onse a mpingo anali komweko. Onani mutuwo |