Machitidwe a Atumwi 21:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo pokhalapo masiku ambiri, anatsika ku Yudeya mneneri, dzina lake Agabu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo pokhalapo masiku ambiri, anatsika ku Yudeya mneneri, dzina lake Agabu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ife tili kumeneko masiku angapo, kudabwera mneneri wina kuchokera ku Yudeya, dzina lake Agabu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Titakhala kumeneko masiku ambiri, kunabwera mneneri wina wochokera ku Yudeya dzina lake Agabu. Onani mutuwo |