Machitidwe a Atumwi 20:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo munali nyali zambiri m'chipinda chapamwamba m'mene tinasonkhanamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo munali nyali zambiri m'chipinda chapamwamba m'mene tinasonkhanamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 M'chipinda cham'mwamba chimene tidaasonkhanamo munali nyale zambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Munali nyale zambiri mʼchipinda chammwamba mʼmene tinasonkhanamo. Onani mutuwo |