Machitidwe a Atumwi 20:34 - Buku Lopatulika34 Mudziwa inu nokha kuti manja anga awa anatumikira zosowa zanga, ndi za iwo akukhala ndi ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Mudziwa inu nokha kuti manja anga awa anatumikira zosowa zanga, ndi za iwo akukhala ndi ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Inu nomwe mukudziŵa kuti manja angaŵa adagwira ntchito kuti ndipeze zimene ine ndi anzanga tinkasoŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Inu nomwe mukudziwa kuti manja angawa ananditumikira kuti tipeze zimene ine ndi anzanga tinkazifuna. Onani mutuwo |