Machitidwe a Atumwi 20:30 - Buku Lopatulika30 ndipo mwa inu nokha adzauka anthu, olankhula zokhotakhota, kupatutsa ophunzira awatsate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 ndipo mwa inu nokha adzauka anthu, olankhula zokhotakhota, kupatutsa ophunzira awatsate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Ngakhale pakati pa inu nomwe, padzauka ena olankhula zonama nkumakopa ophunzira kuti aŵatsate. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Ngakhale pakati pa inu nokha padzapezeka anthu oyankhula zonama ndi cholinga chofuna kukhala ndi ophunzira kuti awatsate. Onani mutuwo |