Machitidwe a Atumwi 20:23 - Buku Lopatulika23 koma kuti Mzimu Woyera andichitira umboni m'mizinda yonse, ndi kunena kuti nsinga ndi zisautso zindilindira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 koma kuti Mzimu Woyera andichitira umboni m'midzi yonse, ndi kunena kuti nsinga ndi zisautso zindilindira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Chokhachi ndikudziŵa kuti Mzimu Woyera wandichenjeza mu mzinda uliwonse kuti ndende ndi mazunzo zikundidikira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Chimene ndikudziwa ndi chakuti Mzimu Woyera wandichenjeza mu mzinda uliwonse kuti ndende ndi mavuto zikundidikira. Onani mutuwo |