Machitidwe a Atumwi 20:20 - Buku Lopatulika20 kuti sindinakubisirani zinthu zopindulira, osazilalikira kwa inu, ndi kukuphunzitsani inu pabwalo ndi m'nyumba zanu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 kuti sindinakubisirani zinthu zopindulira, osazilalikira kwa inu, ndi kukuphunzitsani inu pabwalo ndi m'nyumba zanu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Mukudziŵa kuti sindidakubisireni kanthu kalikonse koti nkukuthandizani. Ndidakulalikirani ndi kukuphunzitsani poyera ndiponso m'nyumba zanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Inu mukudziwa kuti, sindinakubisireni kanthu kalikonse kopindulitsa koma ndinakuphunzitsani poyera komanso nyumba ndi nyumba. Onani mutuwo |