Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 20:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo m'mene tidachokerapo, m'mawa mwake tinafika pandunji pa Kiyo; ndi m'mawa mwake tinangokocheza ku Samo, ndi m'mawa mwake tinafika ku Mileto.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo m'mene tidachokerapo, m'mawa mwake tinafika pandunji pa Kiyo; ndi m'mawa mwake tinangokocheza ku Samo, ndi m'mawa mwake tinafika ku Mileto.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Tidachokanso kumeneko m'chombo, ndipo m'maŵa mwake tidakafika pafupi ndi Kiyo. M'maŵa mwakenso tidawolokera ku Samo, ndipo mkucha wake tidakafika ku Mileto.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Mmawa mwake tinachoka kumeneko pa sitima ya pamadzi ndipo tinafika pafupi ndi Kiyo. Tsiku linalo tinawolokera ku Samo, ndipo tsiku linanso tinafika ku Mileto.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 20:15
3 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene anakomana ndi ife ku Aso, tinamlandira, ndipo tinafika ku Mitilene.


Ndipo pokhala ku Mileto anatuma ku Efeso, naitana akulu a Mpingo.


Erasto anakhalira mu Korinto; koma Trofimo ndamsiya wodwala ku Mileto.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa