Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 20:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo pamene anakomana ndi ife ku Aso, tinamlandira, ndipo tinafika ku Mitilene.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo pamene anakomana ndi ife ku Aso, tinamlandira, ndipo tinafika ku Mitilene.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Pamene iye adakumana nafe ku Aso, adakwera nafe m'chombomo, ndipo tidakafika ku Mitilene.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Pamene anakumana nafe ku Aso tinamutenga ndipo tinapita ku Mitilene.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 20:14
2 Mawu Ofanana  

Koma ife tinatsogolera kunka kungalawa, ndipo tinapita ku Aso, pamenepo tinati timlandire Paulo; pakuti anatipangira chomwecho, koma anati ayenda pamtunda yekha.


Ndipo m'mene tidachokerapo, m'mawa mwake tinafika pandunji pa Kiyo; ndi m'mawa mwake tinangokocheza ku Samo, ndi m'mawa mwake tinafika ku Mileto.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa