Machitidwe a Atumwi 20:13 - Buku Lopatulika13 Koma ife tinatsogolera kunka kungalawa, ndipo tinapita ku Aso, pamenepo tinati timlandire Paulo; pakuti anatipangira chomwecho, koma anati ayenda pamtunda yekha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma ife tinatsogolera kunka kungalawa, ndipo tinapita ku Aso, pamenepo tinati timlandire Paulo; pakuti anatipangira chomwecho, koma anati ayenda pamtunda yekha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ife tidatsogola nkukakwera chombo kupita ku Aso, kumene tinkayembekeza kukatengako Paulo. Iye adaakonza motero, chifukwa adaafuna kudzera pa mtunda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ife tinatsogola kukakwera sitima ya pa madzi kupita ku Aso, kumene tinayembekeza kukatenga Paulo. Iye anakonza motero chifukwa amayenda wapansi. Onani mutuwo |