Machitidwe a Atumwi 20:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo anadza naye mnyamata ali wamoyo, natonthozedwa kwakukulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo anadza naye mnyamata ali wamoyo, natonthozedwa kwakukulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Anthu aja adatenga mnyamata uja ali moyo, ndipo onse adasangalala kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Anthu anatenga mnyamatayo kupita kwawo ali moyo ndipo anatonthozedwa mtima kwambiri. Onani mutuwo |