Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 20:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo potsikirako Paulo, anamgwera namfungatira, nati, Musachite phokoso, pakuti moyo wake ulipo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo potsikirako Paulo, anamgwera namfungatira, nati, Musachite phokoso, pakuti moyo wake ulipo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Pamenepo Paulo adatsika, nadziponya pa mnyamatayo nkumufungatira nati, “Musavutike, ali moyo.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Paulo anatsika, nadziponya pa mnyamatayo, namukumbatira. Paulo anati, “Musadandaule, ali moyo!”

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 20:10
8 Mawu Ofanana  

Ndipo m'mene atalowa, ananena nao, Mubuma ndi kulira bwanji? Mwana sanafe, koma ali m'tulo.


Ndipo pamene Ambuye anamuona, anagwidwa ndi chifundo chifukwa cha iye, nanena naye, Usalire.


Izi anati, ndipo zitatha izi ananena nao, Lazaro bwenzi lathu ali m'tulo; koma ndimuka kukamuukitsa iye tulo take.


Yesu ananena naye, Kodi sindinati kwa iwe, kuti, ngati ukhulupirira, udzaona ulemerero wa Mulungu?


Ndipo mnyamata dzina lake Yutiko anakhala pazenera, wogwidwa nato tulo tatikulu; ndipo pakukhala chifotokozere Paulo, ndipo pogwidwa nato tulo, anagwa posanja pachiwiri, ndipo anamtola wakufa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa