Machitidwe a Atumwi 2:5 - Buku Lopatulika5 Koma anali mu Yerusalemu okhalako Ayuda, amuna opembedza, ochokera kumtundu uliwonse pansi pa thambo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma anali m'Yerusalemu okhalako Ayuda, amuna opembedza, ochokera kumtundu uliwonse pansi pa thambo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsono, m'Yerusalemu muja munali Ayuda ena, anthu okonda Mulungu, ochokera ku maiko onse a pa dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ayuda woopa Mulungu ochokera ku mayiko onse a dziko lapansi ankakhala mu Yerusalemu nthawi imeneyi. Onani mutuwo |