Machitidwe a Atumwi 2:45 - Buku Lopatulika45 Ndipo zimene anali nazo, ndi chuma chao, anazigulitsa, nazigawira kwa onse, monga momwe yense anasowera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Ndipo zimene anali nazo, ndi chuma chao, anazigulitsa, nazigawira kwa onse, monga momwe yense anasowera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 Ankagulitsa minda yao ndi katundu wao, ndalama zake nkumagaŵira onse, malinga ndi kusoŵa kwa aliyense. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 Ankagulitsa minda yawo ndi katundu wawo, ndi kugawira kwa aliyense molingana ndi zosowa zake. Onani mutuwo |