Machitidwe a Atumwi 2:43 - Buku Lopatulika43 Koma panadza mantha pa anthu onse; ndipo zozizwa ndi zizindikiro zambiri zinachitika ndi atumwi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Koma panadza mantha pa anthu onse; ndipo zozizwa ndi zizindikiro zambiri zinachitika ndi atumwi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Anthu onse ankaopa Mulungu poona zozizwitsa ndi zizindikiro zambiri zimene atumwi ankachita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Aliyense ankachita mantha chifukwa cha zodabwitsa ndi zizindikiro zambiri zimene atumwi ankachita. Onani mutuwo |