Machitidwe a Atumwi 2:42 - Buku Lopatulika42 Ndipo anali chikhalire m'chiphunzitso cha atumwi ndi m'chiyanjano, m'kunyema mkate ndi mapemphero. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Ndipo anali chikhalire m'chiphunzitso cha atumwi ndi m'chiyanjano, m'kunyema mkate ndi mapemphero. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Anthuwo ankasonkhana modzipereka kuti amve zimene atumwi ankaphunzitsa. Ankayanjana, ndipo ankadya Mgonero wa Ambuye ndi kupemphera pamodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Iwo ankasonkhana pamodzi kuphunzitsidwa ndi atumwi, pachiyanjano, pachakudya ndi popemphera. Onani mutuwo |