Machitidwe a Atumwi 2:27 - Buku Lopatulika27 Pakuti simudzasiya moyo wanga ku dziko la akufa, kapena simudzapereka Woyera wanu aone chivunde, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Pakuti simudzasiya moyo wanga ku dziko la akufa, kapena simudzapereka Woyera wanu aone chivunde, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 ndikhulupirira kuti simudzandisiya ku Malo a anthu akufa, kapena kulekerera Woyera wanu kuti aole. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Chifukwa simudzasiya moyo wanga kumalo a anthu akufa, ku manda, kapena kulekerera Woyerayo kuti awole. Onani mutuwo |