Machitidwe a Atumwi 2:26 - Buku Lopatulika26 mwa ichi unakondwera mtima wanga, ndipo linasangalala lilime langa; ndipo thupi langanso lidzakhala m'chiyembekezo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 mwa ichi unakondwera mtima wanga, ndipo linasangalala lilime langa; ndipo thupi langanso lidzakhala m'chiyembekezo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Nchifukwa chake mtima wanga udakondwa, ndipo ndinkalankhula mosangalala. Ndithu, ngakhale thupi langa lomwe lidzapumula m'manda, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Chifukwa chake mtima wanga ndi wokondwa ndipo lilime langa likukondwera; thupi langanso lidzakhala ndi chiyembekezo. Onani mutuwo |