Machitidwe a Atumwi 2:25 - Buku Lopatulika25 Pakuti Davide anena za Iye, Ndinaona Mbuye pamaso panga nthawi zonse; chifukwa ali padzanja langa lamanja, kuti ndingasinthike; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Pakuti Davide anena za Iye, Ndinaona Mbuye pamaso panga nthawi zonse; chifukwa ali pa dzanja langa lamanja, kuti ndingasinthike; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 “Paja Davide ponena za Iye adati, ‘Ndinkaona Ambuye Mulungu pamaso panga nthaŵi zonse, pakuti amakhala ku dzanja langa lamanja kuti ndingagwedezeke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Pakuti Davide ananena za Iye kuti, “ ‘Ndinaona Ambuye pamaso panga nthawi zonse. Chifukwa Iye ali kudzanja langa lamanja, Ine sindidzagwedezeka. Onani mutuwo |