Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 2:21 - Buku Lopatulika

21 Ndipo kudzali, kuti yense amene akaitana pa dzina la Ambuye adzapulumutsidwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndipo kudzali, kuti yense amene akaitana pa dzina la Ambuye adzapulumutsidwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Pamenepo aliyense amene adzatama dzina la Ambuye mopemba, adzapulumuka.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Ndipo aliyense amene adzayitana pa dzina la Ambuye adzapulumuka.’

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 2:21
10 Mawu Ofanana  

Pakuti Inu, Ambuye, ndinu wabwino, ndi wokhululukira, ndi wa chifundo chochulukira onse akuitana Inu.


Ndipo kudzachitika kuti aliyense adzaitana pa dzina la Yehova adzapulumutsidwa; pakuti m'phiri la Ziyoni ndi mu Yerusalemu mudzakhala chipulumutso, monga Yehova anatero, ndi mwa otsala amene Yehova adzawaitana.


Chifukwa chake mukani, phunzitsani anthu a mitundu yonse, ndi kuwabatiza iwo m'dzina la Atate, ndi la Mwana, ndi la Mzimu Woyera:


dzuwa lidzasanduka mdima, ndi mwezi udzasanduka mwazi, lisanadze tsiku la Ambuye, lalikulu ndi loonekera.


Ndipo tsopano uchedweranji? Tauka, nubatizidwe ndi kusamba kuchotsa machimo ako, nuitane pa dzina lake.


Ndipo Ambuye anati kwa iye, Tauka, pita ku khwalala lotchedwa Lolunjika, ndipo m'nyumba ya Yudasi ufunse za munthu dzina lake Saulo, wa ku Tariso: pakuti taona, alikupemphera


Koma Ambuye anati kwa iye, Pita; pakuti iye ndiye chotengera changa chosankhika, chakunyamula dzina langa pamaso pa amitundu ndi mafumu ndi ana a Israele;


kwa Mpingo wa Mulungu wakukhala mu Korinto, ndiwo oyeretsedwa mwa Khristu Yesu, oitanidwa akhale oyera mtima, pamodzi ndi onse akuitana pa dzina la Ambuye wathu Yesu Khristu, m'malo monse, ndiye wao, ndi wathu:


Potero tilimbike mtima poyandikira mpando wachifumu wachisomo, kuti tilandire chifundo ndi kupeza chisomo cha kutithandiza nthawi yakusowa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa