Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 19:5 - Buku Lopatulika

5 Pamene anamva ichi, anabatizidwa m'dzina la Ambuye Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Pamene anamva ichi, anabatizidwa m'dzina la Ambuye Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Okhulupirira aja atamva zimenezi, adabatizidwa m'dzina la Ambuye Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Atamva zimenezi, anabatizidwa mʼdzina la Ambuye Yesu.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 19:5
7 Mawu Ofanana  

Ndipo analamulira iwo abatizidwe m'dzina la Yesu Khristu. Pamenepo anampempha iye atsotse masiku.


Koma Petro anati kwa iwo, Lapani, batizidwani yense wa inu m'dzina la Yesu Khristu kuloza ku chikhululukiro cha machimo anu; ndipo mudzalandira mphatso ya Mzimu Woyera.


Koma pamene anakhulupirira Filipo wakulalikira Uthenga Wabwino wa Ufumu wa Mulungu ndi dzina la Yesu Khristu, anabatizidwa, amuna ndi akazi.


pakuti kufikira pamenepo nkuti asanagwe pa wina mmodzi wa iwo; koma anangobatizidwa m'dzina la Ambuye Yesu.


nabatizidwa onse kwa Mose, mumtambo, ndi m'nyanja,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa